Livros cristãos gratuitos para estudos bíblicos sobre salvação, o Espírito Santo, o Tabernáculo e o Apocalipse de João

HOME  |  MAPA DO SITE  |  CONTATO  |  AJUDA    
Estudos da Bíblia Livros Cristãos
Grátis
e-livros Cristãos
Grátis
Sobre Nós
 



 Versão grátis da edição Chichewa 1 do e-livro

 


Kodi mwabadwadi mwatsopano mwa madzi ndi mwa Mzimu Woyera?

  • Formato do livro eletrônico : Acrobat PDF Reader
  • Downloads realizados : 63
  • Sobre este livro
  • Tabela de conteúdos
 

Kulengeza:

Ili ndilo buku loyamba mnthawi yathu lakulalika za 'Uthenga wa bwino wa Madzi ndi Mzimu' mogwirizana kwambiri ndi Malembo.

Kufothokoza:

Ndime yamuthu waukhulu ya m'nkhaniyi ndi "ku Badwanso mwa Madzi ndi Mzimu." Muthuyu wachoka mnkhani yomweyi. Kunenetsa, bukuli likufothokoza tanthauzo lakubadwanso ndi mwamene mungabadwirenso mwa madzi ndi Mzimu mogwirizana ndi Bibulo. Madzi akuimirira ubadizo wa Yesu mu Yordani ndipo Babilo likuti machismo athu tonse anaikidwa pa Yesuyo pamene anabadizidwa ndi Yohane Mbatizi. Yohane ankhaimilira anthu amitundu yosina-siyana anali wambanja la Aloni wa Sembe Wamkhulu. Aloniyo aikha manja ake pa mbuzi yopepetsera machimo a Asiraeli achaka chonse Patsiku la Kupepetsera Machismo. Chinali chinthunzi-thunzi cha zinthu zabwino zikubwera. Kubadizidwa kwa Yesu kukufanizira kuikhapo manja kuja. Yesu anabadizidwa m'njira yoikha manja ku mtsinje wa Yordani uja. Ndiye anachotsa machismo adziko lonse paubadizo Wake ndipo anapachikidwa kuti alipe machimo athu. Koma anthu ambiri sakudziwa nchifukwa chanji Yesu anabadizidwa ndi Yohani mu Yordani. Ubadizo wa Yesu ndiyo nfundo yaikhulu mbukuli, imene singasiyanitsidwe ndi Uthenga wa Bwino wa madzi ndi Mzimu. Tingabadwenso ngati tikhulupirira mu ubadizo wa Yesu ndi Mtanda Wake.

Mau a wosindikiza:

Rev. Paul C. Jong wakhala akulalika uthenga wa madzi ndi Mzimu mdziko lonse lapansi kupitirira zaka makumi awiri. Walembanso mithu yankhani yopitirira pa makumi asanu m'mabuku ake ofunika a chi Kristu, Mithu yaikhului yasandulizidwa mzinenero zikhulu-zikhulu zopitirira makumi anai. Mau ake ndi amphamvu ndi uzimu kotere kuti ambiri owerenga mabukuwa anga badwenso ndi kulandira Mzimo Woyera. Tikusimikiza kuti ili ndilo buku loyamba mnthawi yathu lakulalika za Uthenga wa bwino wa madzi ndi Mzimu mogwirizana kwambiri ndi Malembo.


 
Free Christian eBooks
    Lista de e-livros
    Edição Chichewa 1
 
  • Sobre este livro
  •  
  • Tabela de conteúdos
  •     O que é um e-livro
     
  • Sobre o e-livro
  •  
  • Como ler um e-livro?
  •  
  • FAQ
  •  
  • Ajuda para Download
  •     Leitores de e-livros
     
  • MS Reader 2.0
  •  
  • Acrobat Reader 5.0
  •  

       
    Copyright © 2001 - 2013 The New Life Mission. ALL RIGHTS reserved.